Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 32:19-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. Uposa yani m'kukoma kwako? tsika, nuikidwe ndi osadulidwa.

20. Adzagwa pakati pa iwo ophedwa ndi lupanga, operekedwa kwa lupanga, mkokereko ndi aunyinji ace onse.

21. Amphamvu oposa ali m'kati mwa manda adzanena naye, pamodzi ndi othandiza ace, Anatsikira, agonako osadulidwawo, ophedwa ndi lupanga,

22. Asuri ali komwe ndi msonkhano wace wonse, manda ace amzinga; ophedwa onsewo, adagwa ndi lupanga;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 32