Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 25:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo mau a Yehova anandidzera, akuti,

2. Wobadwa ndi munthu iwe, Lozetsa nkhope yako kwa ana a Amoni, nuwanenere;

3. nunene kwa ana a Amoni, Tamverani mau a Ambuye Yehova, Atero Ambuye Yehova, Popeza unati, Onyo, kunena malo anga opatulika; muja anadetsedwa ndi kunena dziko la Israyeli; muja linapasuka ndi kunena nyumba ya Yuda; muja adalowa kundende;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 25