Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 24:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Momwemo Ezekieli adzakhala kwa inu cizindikilo; umo monse anacitira iye mudzacita ndinu; cikadza ici mudzadziwa kuti Ine ndine Ambuye Yehova.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 24

Onani Ezekieli 24:24 nkhani