Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 23:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iwowa anabvula umarisece wace, anatenga ana ace amuna ndi akazi, namupha iyeyu ndi lupanga; ndi dzina lace linamveka mwa akazi atamcitira maweruzo.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 23

Onani Ezekieli 23:10 nkhani