Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 22:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mwa iwe anapepula atate ndi mai, pakati pa iwe anamcitira mlendo momzunza, mwa iwe anazunza ana amasiye, ndi mkazi wamasiye.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 22

Onani Ezekieli 22:7 nkhani