Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 22:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Monga siliva asungunuka m'kati mwa ng'anjo, momwemo inu mudzasungunuka m'kati mwace; motero mudzadziwa kuti Ine Yehova ndakutsanulirani ukali wanga.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 22

Onani Ezekieli 22:22 nkhani