Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 20:34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzakuturutsani mwa mitundu ya anthu, ndi kukusonkhanitsani m'maiko munabalalikamo ndi dzanja lamphamvu, ndi mkono wotambasuka, ndi ukali wotsanulidwa.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 20

Onani Ezekieli 20:34 nkhani