Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 20:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace uziti kwa nyumba ya Israyeli, Atero Ambuye Yehova, Mudzidetsa kodi monga umo anacitira makolo anu? mucita cigololo kodi kutsata zonyansa zao?

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 20

Onani Ezekieli 20:30 nkhani