Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 20:16-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. popeza ananyoza maweruzo anga, osayenda m'malemba anga, naipsa masabata anga; pakuti mitima yao inatsata mafano ao.

17. Koma diso langa lidawaleka osawaononga, sindinawatha onse m'cipululu.

18. Ndipo ndinati kwa ana ao m'cipululu, Musamayenda m'malemba a atate anu, musawasunga maweruzo ao, kapena kudzidetsa ndi mafano ao;

19. Ine ndine Yehova Mulungu wanu, muziyenda m'malemba anga, ndi kusunga maweruzo anga, ndi kuwacita;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 20