Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 19:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma unazulidwa mwaukali, unaponyedwa pansi ndi mphepo ya kum'mawa, inaumitsa zipatso zace, ndodo zace zolimba zinatyoka ndi kuuma, moto unazitha.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 19

Onani Ezekieli 19:12 nkhani