Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 17:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndidzamphimbanso ndi ukonde wanga, nadzakodwa iye mu msampha wanga; ndipo ndidzadza naye ku Babulo, ndi kunena naye komweko mlandu wa kulakwa kwace anandilakwira nako.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 17

Onani Ezekieli 17:20 nkhani