Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 17:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Farao ndi nkhondo yace yaikuru, ndi khamu lace launyinji, sadzacita pamodzi naye kunkhondo, pakuunda mtumbira, ndi kumanga malinga, kulikha anthu ambiri.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 17

Onani Ezekieli 17:17 nkhani