Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 17:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Uziti tsono kwa nyumba ya mpandukoyi, Simudziwa kodi izi nciani? Uziti, Taonani mfumu ya ku Babulo inadza ku Yerusalemu, nitenga mfumu yace ndi akalonga ace, nibwera nao kuti iye ku Babulo;

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 17

Onani Ezekieli 17:12 nkhani