Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 16:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo popita Ine panali iwepo, ndinakuona ulikubvimvinizika m'mwazi wako. Pamenepo ndinanena ndi iwe m'mwazi wako, Khala ndi moyo, inde ndinati kwa iwe m'mwazi mwako, Khala ndi moyo.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 16

Onani Ezekieli 16:6 nkhani