Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 16:45 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iwe ndiwe mwana wa mako wonyansidwa naye mwamuna wace ndi ana ace, ndipo iwe ndiwe mng'ono wao wa akulu ako akunyansidwa ndi amuna ao ndi ana ao; mai wako ndiye Mhiti, ndi atate wako ndiye M-amori.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 16

Onani Ezekieli 16:45 nkhani