Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 16:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo za kubadwa kwako, tsiku lobadwa iwe sanadula ncofu yako, sanakuyeretsa ndi kukusambitsa ndi madzi, sanakuthira mcere konse, kapena kukukulunga m'nsaru ai.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 16

Onani Ezekieli 16:4 nkhani