Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 14:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo adzakusangalatsani pamene muona njira yao, ndi zocita zao; ndipo mudzadziwa kuti sindinazicita kopanda cifukwa zonse ndinazicita momwemo, ati Ambuye Yehova.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 14

Onani Ezekieli 14:23 nkhani