Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 12:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wobadwa ndi munthu iwe, ukhala pakati pa nyumba yampanduko, yokhala nao maso akuonera, koma osaona; ndi makutu akumvera, koma osamva; pakuti iwo ndiwo nyumba yampanduko.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 12

Onani Ezekieli 12:2 nkhani