Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 12:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ndidzawasiya owerengeka apulumuke lupanga, ndi njala, ndi mliri, kuti afotokoze zonyansa zao kwa amitundu kumene afikako; ndipo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 12

Onani Ezekieli 12:16 nkhani