Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 11:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace uziti, Atero Yehova Mulungu, Ndidzakumemezani ku mitundu ya anthu, ndi kukusonkhanitsani mucoke m'maiko m'mene munabalalikiramo, ndipo ndidzakuninkhani dziko la Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 11

Onani Ezekieli 11:17 nkhani