Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 11:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, pakunenera ine, anamwalira Pelatiya mwana wa Benaya. Pamenepo ndinagwa nkhope yanga pansi, ndi kupfuula ndi mau akuru, ndi kuti, Kalanga ine, Yehova Mulungu! mudzatsiriza kodi otsala a Israyeli?

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 11

Onani Ezekieli 11:13 nkhani