Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 1:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Maonekedwe a njingazi ndi mapangidwe ao ananga mawalidwe a berulo; ndi izi zinai zinafanana mafaniziro ao; ndi maonekedwe ao ndi mapangidwe ao anali ngati njinga ziwiri zopingasitsana.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 1

Onani Ezekieli 1:16 nkhani