Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 8:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinawatumiza kwa Ido mkuru, ku malo dzina lace Kasifiya; ndinalooganso m'kamwa mwao mau akunena kwa Ido, ndi kwa abale ace Anetini, pa malo paja Kasifiya, kuti azibwera nao kwa ife otumikira za nyumba ya Mulungu wathu.

Werengani mutu wathunthu Ezara 8

Onani Ezara 8:17 nkhani