Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 7:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Zitatha izi tsono, pokhala mfumu Aritasasta mfumu ya Perisiya, anadza Ezara mwana wa Seraya, mwana wa Azariya, mwana wa Hilikiya,

2. mwana wa Salumu, mwana wa Zadoki, mwana wa Ahitubu,

3. mwana wa Amariya, mwana wa Azariya, mwana wa Meraioti,

4. mwana wa Zerahiya, mwana wa Uzi, mwana wa Buki,

Werengani mutu wathunthu Ezara 7