Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 4:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Adziwe mfumu kuti, Ayuda adakwerawo ocokera kwanu atifikira ife ku Yerusalemu, alikumanga mudzi uja wopanduka ndi woipa, alikutsiriza malinga ace, nalumikiza maziko ace.

Werengani mutu wathunthu Ezara 4

Onani Ezara 4:12 nkhani