Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 3:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anaimirira pamodzi Yesuwa ndi ana ace ndi abale ace, Kadimiyeli ndi ana ace, ana a Yuda, kuyang'anira ogwira nchito m'nyumba ya Yehova, ana a Henadadi ndi ana ao ndi abale ao Alevi.

Werengani mutu wathunthu Ezara 3

Onani Ezara 3:9 nkhani