Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 3:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anaperekanso ndarama kwa amisiri a miyala, ndi a mitengo; ndi cakudya, ndi cakumwa, ndi mafuta, kwa a ku Sidoni, ndi a ku Turo, kuti atenge mikungudza ku Lebano, kufika nayo ku nyanja ku Yopa, monga adawalola Koresi mfumu ya Babulo.

Werengani mutu wathunthu Ezara 3

Onani Ezara 3:7 nkhani