Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 3:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anathirirana mang'ombe, kulemekeza ndi kuyamika Yehova, ndi kuti, Pakuti ndiye wabwino, pakuti cifundo cace ncosalekeza pa Israyeli. Napfuula anthu onse ndi cipfuu cacikuru, pomlemekeza Yehova; popeza adamanga maziko a nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu Ezara 3

Onani Ezara 3:11 nkhani