Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 2:7-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Ana a Elamu, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi asanu ndi anai.

8. Ana a Zatu, mazana asanu ndi anai mphambu makumi anai kudza asanu.

9. Ana a Zakai, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi asanu ndi limodzi.

10. Ana a Bani, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza awiri.

11. Ana a Bebai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

12. Ana a Asigadi, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi awiri ndi awiri.

13. Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi mmodzi.

14. Ana a Bigivai, zikwi ziwiri mphambu makumi asanu kudza asanu ndi mmodzi.

15. Ana a Adini, mazana anai mphambu makumi asanu kudza anai.

16. Ana a Ateri, a Hezekiya, makumi asanu ndi anai mphambu asanu ndi atatu.

17. Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza atatu.

18. Ana a Yora, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.

Werengani mutu wathunthu Ezara 2