Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 2:47-58 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

47. ana a Gideli, ana a Gahari, ana a Reaya,

48. ana a Rezini, ana a Nekoda, ana a Gazamu,

49. ana a Uza, ana a Paseya, ana a Besai,

50. ana a Asina, ana a Mehunimu, ana a Nefusimu,

51. ana a Bakabuku, ana a Hakufa, ana a Haruri,

52. ana a Baziluti, ana a Mehida, ana a Harisa,

53. ana a Barikosi, ana a Siseri, ana a Tama,

54. ana a Neziya, ana a Hatifa.

55. Ana a akapolo a Solomo: ana a Sotai, ana a Sofereti, ana a Peruda,

56. ana a Yaala, ana a Darikoni, ana a Gideli,

57. ana a Sefatiya, ana a Hatili, ana a Pokereti wa Zebaimu, ana a Ami.

58. Anetini onse, ndi ana a akapolo a Solomo, ndiwo mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai kudza awiri.

Werengani mutu wathunthu Ezara 2