Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 2:42-59 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

42. Ana a odikira: ana a Sabumu, ana a Ateri, ana a Talimoni, ana a Akubu, ana a Hatita, ana a Sobai, onse pamodzi ndiwo zana limodzi mphambu makumi atatu kudza asanu ndi anai.

43. Anetini: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti,

44. ana a Kerosi, ana a Siaha, ana a Padoni,

45. ana a Lebano, ana a Hagaba, ana a Akubu,

46. ana a Hagabu, ana a Salimai, ana a Hanani,

47. ana a Gideli, ana a Gahari, ana a Reaya,

48. ana a Rezini, ana a Nekoda, ana a Gazamu,

49. ana a Uza, ana a Paseya, ana a Besai,

50. ana a Asina, ana a Mehunimu, ana a Nefusimu,

51. ana a Bakabuku, ana a Hakufa, ana a Haruri,

52. ana a Baziluti, ana a Mehida, ana a Harisa,

53. ana a Barikosi, ana a Siseri, ana a Tama,

54. ana a Neziya, ana a Hatifa.

55. Ana a akapolo a Solomo: ana a Sotai, ana a Sofereti, ana a Peruda,

56. ana a Yaala, ana a Darikoni, ana a Gideli,

57. ana a Sefatiya, ana a Hatili, ana a Pokereti wa Zebaimu, ana a Ami.

58. Anetini onse, ndi ana a akapolo a Solomo, ndiwo mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai kudza awiri.

59. Ndipo okwera kucokera ku Telemela, Teleharisa, Kerubi, Adana, Imeri, ndi awa, koma sanakhoza kuchula nyumba za makolo ao ndi mbumba zao ngati ali Aisrayeli:

Werengani mutu wathunthu Ezara 2