Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 2:39-49 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

39. Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.

40. Alevi: ana a Yesuwa, ndi Kadimiyeli, ndiwo a ana a Hodariya, makumi asanu ndi awiri mphambu anai.

41. Oyimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

42. Ana a odikira: ana a Sabumu, ana a Ateri, ana a Talimoni, ana a Akubu, ana a Hatita, ana a Sobai, onse pamodzi ndiwo zana limodzi mphambu makumi atatu kudza asanu ndi anai.

43. Anetini: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti,

44. ana a Kerosi, ana a Siaha, ana a Padoni,

45. ana a Lebano, ana a Hagaba, ana a Akubu,

46. ana a Hagabu, ana a Salimai, ana a Hanani,

47. ana a Gideli, ana a Gahari, ana a Reaya,

48. ana a Rezini, ana a Nekoda, ana a Gazamu,

49. ana a Uza, ana a Paseya, ana a Besai,

Werengani mutu wathunthu Ezara 2