37. Ana a lmneri, cikwi cimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.
38. Ana a Pasuru, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.
39. Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.
40. Alevi: ana a Yesuwa, ndi Kadimiyeli, ndiwo a ana a Hodariya, makumi asanu ndi awiri mphambu anai.
41. Oyimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.
42. Ana a odikira: ana a Sabumu, ana a Ateri, ana a Talimoni, ana a Akubu, ana a Hatita, ana a Sobai, onse pamodzi ndiwo zana limodzi mphambu makumi atatu kudza asanu ndi anai.
43. Anetini: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti,
44. ana a Kerosi, ana a Siaha, ana a Padoni,
45. ana a Lebano, ana a Hagaba, ana a Akubu,
46. ana a Hagabu, ana a Salimai, ana a Hanani,
47. ana a Gideli, ana a Gahari, ana a Reaya,
48. ana a Rezini, ana a Nekoda, ana a Gazamu,
49. ana a Uza, ana a Paseya, ana a Besai,
50. ana a Asina, ana a Mehunimu, ana a Nefusimu,
51. ana a Bakabuku, ana a Hakufa, ana a Haruri,