Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 2:36-55 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

36. Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.

37. Ana a lmneri, cikwi cimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.

38. Ana a Pasuru, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.

39. Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.

40. Alevi: ana a Yesuwa, ndi Kadimiyeli, ndiwo a ana a Hodariya, makumi asanu ndi awiri mphambu anai.

41. Oyimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

42. Ana a odikira: ana a Sabumu, ana a Ateri, ana a Talimoni, ana a Akubu, ana a Hatita, ana a Sobai, onse pamodzi ndiwo zana limodzi mphambu makumi atatu kudza asanu ndi anai.

43. Anetini: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti,

44. ana a Kerosi, ana a Siaha, ana a Padoni,

45. ana a Lebano, ana a Hagaba, ana a Akubu,

46. ana a Hagabu, ana a Salimai, ana a Hanani,

47. ana a Gideli, ana a Gahari, ana a Reaya,

48. ana a Rezini, ana a Nekoda, ana a Gazamu,

49. ana a Uza, ana a Paseya, ana a Besai,

50. ana a Asina, ana a Mehunimu, ana a Nefusimu,

51. ana a Bakabuku, ana a Hakufa, ana a Haruri,

52. ana a Baziluti, ana a Mehida, ana a Harisa,

53. ana a Barikosi, ana a Siseri, ana a Tama,

54. ana a Neziya, ana a Hatifa.

55. Ana a akapolo a Solomo: ana a Sotai, ana a Sofereti, ana a Peruda,

Werengani mutu wathunthu Ezara 2