28. Anthu a ku Beteli ndi Ai, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.
29. Ana a Nebo, makumi asanu mphambu awiri.
30. Ana a Magabisi, zana limodzi mphambu makumi asanu kudza asanu ndi mmodzi.
31. Ana a Elamu wina, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi asanu ndi anai.