Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 2:27-41 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

27. Anthu a Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

28. Anthu a ku Beteli ndi Ai, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.

29. Ana a Nebo, makumi asanu mphambu awiri.

30. Ana a Magabisi, zana limodzi mphambu makumi asanu kudza asanu ndi mmodzi.

31. Ana a Elamu wina, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi asanu ndi anai.

32. Ana a Harimu, mazana atatu mphambu makumi awiri.

33. Ana a Lodi, Hadidi, ndi Ono, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi awiri kudza asanu.

34. Ana a Yeriko, mazana atatu mphambu makumi anai kudza asanu.

35. Ana a Senai, zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.

36. Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.

37. Ana a lmneri, cikwi cimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.

38. Ana a Pasuru, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.

39. Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.

40. Alevi: ana a Yesuwa, ndi Kadimiyeli, ndiwo a ana a Hodariya, makumi asanu ndi awiri mphambu anai.

41. Oyimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

Werengani mutu wathunthu Ezara 2