26. Ana a Rama ndi Gaba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.
27. Anthu a Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.
28. Anthu a ku Beteli ndi Ai, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.
29. Ana a Nebo, makumi asanu mphambu awiri.
30. Ana a Magabisi, zana limodzi mphambu makumi asanu kudza asanu ndi mmodzi.
31. Ana a Elamu wina, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi asanu ndi anai.
32. Ana a Harimu, mazana atatu mphambu makumi awiri.
33. Ana a Lodi, Hadidi, ndi Ono, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi awiri kudza asanu.
34. Ana a Yeriko, mazana atatu mphambu makumi anai kudza asanu.
35. Ana a Senai, zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.
36. Ansembe: ana a Yedaya, a nyumba ya Yesuwa, mazana asanu ndi anai mphambu makumi asanu ndi awiri kudza atatu.
37. Ana a lmneri, cikwi cimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.
38. Ana a Pasuru, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.
39. Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.
40. Alevi: ana a Yesuwa, ndi Kadimiyeli, ndiwo a ana a Hodariya, makumi asanu ndi awiri mphambu anai.
41. Oyimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.
42. Ana a odikira: ana a Sabumu, ana a Ateri, ana a Talimoni, ana a Akubu, ana a Hatita, ana a Sobai, onse pamodzi ndiwo zana limodzi mphambu makumi atatu kudza asanu ndi anai.
43. Anetini: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti,
44. ana a Kerosi, ana a Siaha, ana a Padoni,
45. ana a Lebano, ana a Hagaba, ana a Akubu,