20. Ana a Gibara, makumi asanu ndi anai mphambu asanu.
21. Ana a Betelehemu zana limodzi mphambu makumi awiri kudza atatu.
22. Anthu a ku Netofa, makumi asanu mphambu asanu ndi mmodzi.
23. Anthu a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.