Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 2:10-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Ana a Bani, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza awiri.

11. Ana a Bebai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

12. Ana a Asigadi, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi awiri ndi awiri.

13. Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi mmodzi.

14. Ana a Bigivai, zikwi ziwiri mphambu makumi asanu kudza asanu ndi mmodzi.

15. Ana a Adini, mazana anai mphambu makumi asanu kudza anai.

16. Ana a Ateri, a Hezekiya, makumi asanu ndi anai mphambu asanu ndi atatu.

17. Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza atatu.

18. Ana a Yora, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.

19. Ana a Hasumu, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.

20. Ana a Gibara, makumi asanu ndi anai mphambu asanu.

21. Ana a Betelehemu zana limodzi mphambu makumi awiri kudza atatu.

22. Anthu a ku Netofa, makumi asanu mphambu asanu ndi mmodzi.

23. Anthu a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

24. Ana a Azimaveti, makumi anai mphambu awiri.

Werengani mutu wathunthu Ezara 2