10. Ana a Bani, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza awiri.
11. Ana a Bebai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.
12. Ana a Asigadi, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi awiri ndi awiri.
13. Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi mmodzi.