Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 2:10-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Ana a Bani, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza awiri.

11. Ana a Bebai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

12. Ana a Asigadi, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi awiri ndi awiri.

13. Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi mmodzi.

Werengani mutu wathunthu Ezara 2