Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 10:28-35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. Ndi a ana a Bebai: Yehohanana, Hananiya, Zabai, Atilai.

29. Ndi a ana a Bani: Mesulamu, Makuli, ndi Adaya, Yasubi, ndi Seali, Yeremoti.

30. Ndi a ana a Pahati: Moabu, Adina, ndi Kelali, Benaya, Maseya, Mataniya, Bezaleli, ndi Binui, ndi Manase.

31. Ndi a ana a Harimu: Eliezere, Isiya, Malikiya, Semaya, Simeoni,

32. Benjamini, Maluki, Semariya.

33. A ana a Hasumu: Matenai, Matata. Zabadi, Elifeleti, Yeremai, Manase, Simei.

34. A ana a Bani: Madai, Amiramu, ndi Ueli,

35. Benaya, Bedeya, Kelui,

Werengani mutu wathunthu Ezara 10