Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 10:26-44 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

26. Ndi a ana a Elamu: Mataniya, Zekariya, ndi Yehieli, ndi Abidi, ndi Yeremoti, ndi Eliya.

27. Ndi a ana a Zatu: Elioenai, Eliasibi, Mataniya, ndi Yeremoti, ndi Zabadi, ndi Aziza.

28. Ndi a ana a Bebai: Yehohanana, Hananiya, Zabai, Atilai.

29. Ndi a ana a Bani: Mesulamu, Makuli, ndi Adaya, Yasubi, ndi Seali, Yeremoti.

30. Ndi a ana a Pahati: Moabu, Adina, ndi Kelali, Benaya, Maseya, Mataniya, Bezaleli, ndi Binui, ndi Manase.

31. Ndi a ana a Harimu: Eliezere, Isiya, Malikiya, Semaya, Simeoni,

32. Benjamini, Maluki, Semariya.

33. A ana a Hasumu: Matenai, Matata. Zabadi, Elifeleti, Yeremai, Manase, Simei.

34. A ana a Bani: Madai, Amiramu, ndi Ueli,

35. Benaya, Bedeya, Kelui,

36. Vaniya, Meremoti, Eliasibi,

37. Mataniya, Matenai, ndi Yasu,

38. ndi Bani, ndi Binui, Simei,

39. ndi Selemiya, ndi Natani, ndi Adaya,

40. Makinadebai, Sasai, Sarai,

41. Azareli, ndi Seleimiya, Semariya,

42. Salumu, Amariya, Yosefe.

43. A ana a Nebo: Yeieli, Matitiya, Zabadi, Zebina, Ido, ndi Yoeli, Banaya,

44. Awa onse adatenga akazi acilendo, ndi ena a iwowa anali ndi akazi amene adawabalira ana.

Werengani mutu wathunthu Ezara 10