Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 10:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anthu otengedwa ndende anacita cotero. Ndi Ezara wansembe, ndi anthu akuru a nyumba za makolo, monga mwa nyumba za makolo ao, iwo onse ochulidwa maina ao anasankhidwa, nakhala pansi tsiku loyamba la mwezi wakhumi kufunsa za mlanduwu.

Werengani mutu wathunthu Ezara 10

Onani Ezara 10:16 nkhani