Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Estere 8:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mfumu Ahaswero anati kwa mkazi wamkuru Estere, ndi kwa Moredekai Myuda, Taonani, ndampatsa Estere nyumba ya Hamani, ndi iyeyu anampacika pamtanda, cifukwa anaturutsa dzanja lace pa Avuda,

Werengani mutu wathunthu Estere 8

Onani Estere 8:7 nkhani