Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Estere 8:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi m'maiko monse, ndi m'midzi yonse, mudafika mau a mfumu ndi lamulo lace, Ayuda anali nako kukondwera ndi cimwemwe, madyerero ndi tsiku lokoma. Ndipo ambiri a mitundu ya anthu a m'dziko anasanduka Ayuda; pakuti kuopsa kwa Ayuda kudawagwera.

Werengani mutu wathunthu Estere 8

Onani Estere 8:17 nkhani