Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Estere 6:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nalowa Hamani. Ndipo mfumu inati kwa iye, Kodi amcitire ciani munthu amene mfumu ikondwera kumcitira ulemu? Ndipo Hamani anati mumtima mwace, Ndaniyo mfumu ikondwera kumcitira ulemu koposa ine?

Werengani mutu wathunthu Estere 6

Onani Estere 6:6 nkhani