Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Estere 4:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ukakhala cete konse tsopano lino, cithandizo ndi cipulumutso zidzafuma kwina; koma iwe ndi nyumba ya atate wako mudzaonongeka; ndipo kaya, kapena walowera ufumu cifukwa ca nyengo yonga iyi.

Werengani mutu wathunthu Estere 4

Onani Estere 4:14 nkhani