Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 7:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Atero Yehova, Ndi ici udzadziwa kuti Ine ndine Yehova: taonani, ndidzapanda madzi ali m'nyanja ndi ndodo iri m'dzanja langa, ndipo adzasanduka mwazi.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 7

Onani Eksodo 7:17 nkhani