Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 6:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo maina a ana amuna a Levi, mwa kubadwa kwao ndiwo: Gerisoni, ndi Kohati, ndi Merari; ndipo zaka za moyo wa Levi ndizo zana limodzi mphambu makumi atatu kudza zisanu ndi ziwiri.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 6

Onani Eksodo 6:16 nkhani