Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 32:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali m'mawa mwace, kuti Mose anati kwa anthu, Mwacimwa kucimwa kwakukulu; koma ndikwera kwa Yehova tsopano, kapena ndidzacita cotetezera ucimo wanu.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 32

Onani Eksodo 32:30 nkhani